1Yehova akulamulira,
2Mʼziyoni wamkulu ndi Yehova;
3Anthu atamande dzina lanu lalikulu ndi loopsa kwambiri,
4Mfumu yamphamvu, iyo imakonda chilungamo
5Kwezani Yehova Mulungu wathu
6Mose ndi Aaroni anali ena mwa ansembe ake,
7Iye anayankhula nawo kuchokera mʼchipilala cha mtambo;
8Inu Yehova Mulungu wathu,
9Kwezani Yehova Mulungu wathu