1Imbirani Yehova nyimbo yatsopano,
2Yehova waonetsa chipulumutso chake
3Iye wakumbukira chikondi chake
4Fuwulani mwachimwemwe kwa Yehova, dziko lonse lapansi,
5Imbirani Yehova nyimbo ndi zeze,
6ndi malipenga ndi kuliza kwa nyanga ya nkhosa yayimuna
7Nyanja ikokome pamodzi ndi zonse zili mʼmenemo,
8Mitsinje iwombe mʼmanja mwawo,
9izo ziyimbe pamaso pa Yehova,