1Yehova akulamulira, dziko lapansi lisangalale;
2Mitambo ndi mdima waukulu zamuzungulira;
3Moto umapita patsogolo pake
4Zingʼaningʼani zake zimawalitsa dziko lonse;
5Mapiri amasungunuka ngati phula pamaso pa Yehova,
6Mayiko akumwamba amalengeza za chilungamo chake,
7Onse amene amalambira mafano osema amachititsidwa manyazi,
8Ziyoni akumva ndipo akukondwera,
9Pakuti Inu Yehova ndi Wammwambamwamba pa dziko lonse lapansi;
10Iwo amene amakonda Yehova adane ndi zoyipa
11Kuwala kumafika pa anthu olungama,
12Kondwerani mwa Yehova Inu olungama