We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 96

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 95 Masalimo Masalimo 97 →

1Imbirani Yehova nyimbo yatsopano;

2Imbirani Yehova, tamandani dzina lake;

3Lengezani ulemerero wake pakati pa mayiko,

4Pakuti wamkulu ndi Yehova ndipo ndi woyenera kwambiri kumutamanda;

5Pakuti milungu yonse ya anthu a mitundu ina ndi mafano,

6Ulemu ndi ufumu zili pamaso pake,

7Perekani kwa Yehova, inu mabanja a anthu a mitundu ina,

8Perekani kwa Yehova ulemerero woyenera dzina lake;

9Lambirani Yehova mu ulemerero wa chiyero chake;

10Nenani pakati pa mitundu ya anthu, “Yehova akulamulira.”

11Mayiko akumwamba asangalale, dziko lapansi likondwere;

12minda ikondwere pamodzi ndi chilichonse chili mʼmenemo.

13idzayimba pamaso pa Yehova,

← Masalimo 95 Masalimo Masalimo 97 →