1Imbirani Yehova nyimbo yatsopano;
2Imbirani Yehova, tamandani dzina lake;
3Lengezani ulemerero wake pakati pa mayiko,
4Pakuti wamkulu ndi Yehova ndipo ndi woyenera kwambiri kumutamanda;
5Pakuti milungu yonse ya anthu a mitundu ina ndi mafano,
6Ulemu ndi ufumu zili pamaso pake,
7Perekani kwa Yehova, inu mabanja a anthu a mitundu ina,
8Perekani kwa Yehova ulemerero woyenera dzina lake;
9Lambirani Yehova mu ulemerero wa chiyero chake;
10Nenani pakati pa mitundu ya anthu, “Yehova akulamulira.”
11Mayiko akumwamba asangalale, dziko lapansi likondwere;
12minda ikondwere pamodzi ndi chilichonse chili mʼmenemo.
13idzayimba pamaso pa Yehova,