1Bwerani, tiyeni timuyimbire Yehova mwachimwemwe,
2Tiyeni tibwere pamaso pake ndi chiyamiko
3Pakuti Yehova ndi Mulungu wamkulu,
4Mʼmanja mwake muli maziko ozama a dziko lapansi,
5Nyanja ndi yake, pakuti anayilenga ndi Iye,
6Bwerani, tiyeni tiwerame pomulambira,
7pakuti Iye ndiye Mulungu wathu
8musawumitse mitima yanu monga momwe munachitira pa Meriba,
9Kumene makolo anu anandiyesa ndi kundiputa,
10Kwa zaka makumi anayi ndinali wokwiya ndi mʼbado umenewo;
11Choncho ndili chikwiyire, ndinalumbira kuti,