We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 94

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 93 Masalimo Masalimo 95 →

1Inu Yehova, ndinu Mulungu wobwezera chilango,

2Nyamukani, Inu woweruza wa dziko lapansi;

3Kodi mpaka liti anthu oyipa Inu Yehova,

4Amakhuthula mawu onyada;

5Amaphwanya anthu anu, Inu Yehova;

6Amaphanso amayi a masiye ndi alendo okhala nawo mʼdziko;

7Iwo amati, “Yehova sakuona;

8Samalani, inu anthu opanda nzeru pakati pa anthu;

9Kodi Iye amene anapanga khutu sangathe kumva?

10Kodi Iye amene amalangiza mitundu ya anthu sangathenso kulanga?

11Yehova amadziwa maganizo a munthu;

12Wodala munthu amene Inu Yehova mumamulangiza,

13mumamupumitsa pa nthawi ya mavuto,

14Pakuti Yehova sadzawakana anthu ake;

15Chiweruzo chidzakhazikikanso pa chilungamo,

16Ndani adzadzuka chifukwa cha ine kulimbana ndi anthu oyipa?

17Yehova akanapanda kundithandiza,

18Ndikanena kuti, “Phazi langa likuterereka,”

19Pamene nkhawa inakula mʼkati mwanga,

20Kodi mpando waufumu woyipa ungathe kugwirizana nanu

21Iwo amasonkhana pamodzi kulimbana ndi wolungama

22Koma Yehova wakhala linga langa,

23Iye adzawabwezera chifukwa cha machimo awo

← Masalimo 93 Masalimo Masalimo 95 →