1Yehova akulamulira, wavala ulemerero;
2Mpando wanu waufumu unakhazikika kalekale;
3Nyanja zakweza Inu Yehova,
4Yehova ndi wamphamvu kupambana mkokomo wa madzi ambiri,
5Malamulo anu Yehova ndi osasinthika;
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja
1Yehova akulamulira, wavala ulemerero;
2Mpando wanu waufumu unakhazikika kalekale;
3Nyanja zakweza Inu Yehova,
4Yehova ndi wamphamvu kupambana mkokomo wa madzi ambiri,
5Malamulo anu Yehova ndi osasinthika;