1Nʼkwabwino kutamanda Yehova
2Kulengeza chikondi chanu mmawa,
3kuyimbira nyimbo choyimbira cha zingwe khumi
4Pakuti Inu mumandisangalatsa ndi ntchito zanu, Inu Yehova;
5Ndi yayikuludi ntchito yanu Yehova,
6Munthu wopanda nzeru sadziwa,
7kuti ngakhale anthu oyipa aphuka ngati udzu
8Koma Inu Yehova, ndinu wokwezedwa kwamuyaya.
9Zoonadi adani anu Yehova,
10Inu mwakweza nyanga yanga ngati nyanga ya njati;
11Maso anga aona kugonjetsedwa kwa olimbana nane,
12Anthu olungama adzaphuka ngati mtengo wa mgwalangwa,
13odzalidwa mʼnyumba ya Yehova,
14Iwo adzaberekabe zipatso mu ukalamba wawo,
15kulengeza kuti, “Yehova ndi wolungama;