We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 92

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 91 Masalimo Masalimo 93 →

1Nʼkwabwino kutamanda Yehova

2Kulengeza chikondi chanu mmawa,

3kuyimbira nyimbo choyimbira cha zingwe khumi

4Pakuti Inu mumandisangalatsa ndi ntchito zanu, Inu Yehova;

5Ndi yayikuludi ntchito yanu Yehova,

6Munthu wopanda nzeru sadziwa,

7kuti ngakhale anthu oyipa aphuka ngati udzu

8Koma Inu Yehova, ndinu wokwezedwa kwamuyaya.

9Zoonadi adani anu Yehova,

10Inu mwakweza nyanga yanga ngati nyanga ya njati;

11Maso anga aona kugonjetsedwa kwa olimbana nane,

12Anthu olungama adzaphuka ngati mtengo wa mgwalangwa,

13odzalidwa mʼnyumba ya Yehova,

14Iwo adzaberekabe zipatso mu ukalamba wawo,

15kulengeza kuti, “Yehova ndi wolungama;

← Masalimo 91 Masalimo Masalimo 93 →