1Iye amene amakhala mu mthunzi wa Wammwambamwamba
2Ndidzanena za Yehova, “Iye ndiye pothawira panga ndi linga langa,
3Ndithu, Iye adzakupulumutsa ku msampha wa mlenje
4Adzakuphimba ndi nthenga zake,
5Sudzachita mantha ndi zoopsa za usiku,
6kapena mliri umene umayenda mu mdima,
7Anthu 1,000 atha kufa pambali pako,
8Udzapenya ndi maso ako
9Pakuti wasankha Wammwambamwamba kukhala malo ako okhalamo;
10Choncho palibe choyipa chimene chidzakugwera,
11Pakuti adzalamulira angelo ake za iwe,
12ndipo adzakunyamula ndi manja awo,
13Udzapondaponda mkango ndi njoka,
14“Chifukwa iye amandikonda,” akutero Yehova, “Ndidzamulanditsa;
15Adzandiyitana, ndipo ndidzamuyankha;
16Ndidzamupatsa moyo wautali