We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 90

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 89 Masalimo Masalimo 91 →

1Ambuye, mwakhala muli malo athu okhalamo

2Mapiri asanabadwe,

3Inu mumabwezera anthu ku fumbi,

4Pakuti zaka 1,000 pamaso panu

5Inu mumasesa anthu mʼtulo ta imfa,

6ngakhale kuti mmawa umaphuka watsopano,

7Ife tathedwa ndi mkwiyo wanu;

8Mwayika mphulupulu zathu pamaso panu,

9Masiku athu onse amatha ali pansi pa ukali wanu;

10Kuchuluka kwa masiku athu ndi 70,

11Kodi ndani amadziwa mphamvu ya mkwiyo wanu?

12Tiphunzitseni kuwerenga masiku athu molondola,

13Lezani mtima Inu Yehova! Kodi mudzatikwiyira mpaka liti?

14Mutikhutitse mmawa ndi chikondi chanu chosatha,

15Tisangalatseni masiku ambiri monga masiku amene mwatisautsa,

16Ntchito zanu zionetsedwe kwa atumiki anu,

17Kukoma mtima kwa Ambuye Mulungu wathu kukhale pa ife;

← Masalimo 89 Masalimo Masalimo 91 →