1Fuwulani kwa Yehova mwachimwemwe, inu dziko lonse lapansi.
2Mulambireni Yehova mosangalala;
3Dziwani kuti Yehova ndi Mulungu.
4Lowani ku zipata zake ndi chiyamiko
5Pakuti Yehova ndi wabwino ndipo chikondi chake ndi chamuyaya;
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja
1Fuwulani kwa Yehova mwachimwemwe, inu dziko lonse lapansi.
2Mulambireni Yehova mosangalala;
3Dziwani kuti Yehova ndi Mulungu.
4Lowani ku zipata zake ndi chiyamiko
5Pakuti Yehova ndi wabwino ndipo chikondi chake ndi chamuyaya;