1Ndidzayimba za chikondi ndi chiweruzo chanu cholungama;
2Ndidzatsata njira yolungama;
3Sindidzayika chinthu chilichonse choyipa
4Anthu a mtima wokhota adzakhala kutali ndi ine;
5Aliyense wosinjirira mnansi wake mseri
6Maso anga adzakhala pa okhulupirika mʼdziko,
7Aliyense wochita chinyengo
8Mmawa uliwonse ndidzatontholetsa anthu