1Yehova imvani pemphero langa;
2Musandibisire nkhope yanu
3Pakuti masiku anga akupita ngati utsi;
4Mtima wanga wakanthidwa ndipo ukufota ngati udzu;
5Chifukwa cha kubuwula kwanga kofuwula
6Ndili ngati kadzidzi wa ku chipululu,
7Ndimagona osapeza tulo; ndakhala
8Tsiku lonse adani anga amandichita chipongwe;
9Pakuti ndimadya phulusa ngati chakudya changa
10chifukwa cha ukali wanu waukulu,
11Masiku anga ali ngati mthunzi wa kumadzulo;
12Koma Inu Yehova, muli pa mpando wanu waufumu kwamuyaya;
13Inu mudzadzuka ndi kuchitira chifundo Ziyoni
14Pakuti miyala yake ndi yokondedwa kwa atumiki anu;
15Mitundu ya anthu idzaopa dzina la Yehova,
16Pakuti Yehova adzamanganso Ziyoni
17Iye adzayankha pemphero la anthu otayika;
18Zimenezi zilembedwe chifukwa cha mibado ya mʼtsogolo,
19“Yehova anayangʼana pansi kuchokera ku malo ake opatulika mmwamba,
20kuti amve kubuwula kwa anthu a mʼndende,
21Kotero dzina la Yehova lidzalengezedwa mu Ziyoni
22pamene mitundu ya anthu ndi maufumu
23Iye anathyola mphamvu zanga pa nthawi ya moyo wanga;
24Choncho Ine ndinati:
25Pachiyambi Inu munakhazikitsa maziko a dziko lapansi
26Izi zidzatha, koma Inu mudzakhalapo;
27Koma Inu simusintha,
28Ana a atumiki anu adzakhala pamaso panu;