We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 102

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 101 Masalimo Masalimo 103 →

1Yehova imvani pemphero langa;

2Musandibisire nkhope yanu

3Pakuti masiku anga akupita ngati utsi;

4Mtima wanga wakanthidwa ndipo ukufota ngati udzu;

5Chifukwa cha kubuwula kwanga kofuwula

6Ndili ngati kadzidzi wa ku chipululu,

7Ndimagona osapeza tulo; ndakhala

8Tsiku lonse adani anga amandichita chipongwe;

9Pakuti ndimadya phulusa ngati chakudya changa

10chifukwa cha ukali wanu waukulu,

11Masiku anga ali ngati mthunzi wa kumadzulo;

12Koma Inu Yehova, muli pa mpando wanu waufumu kwamuyaya;

13Inu mudzadzuka ndi kuchitira chifundo Ziyoni

14Pakuti miyala yake ndi yokondedwa kwa atumiki anu;

15Mitundu ya anthu idzaopa dzina la Yehova,

16Pakuti Yehova adzamanganso Ziyoni

17Iye adzayankha pemphero la anthu otayika;

18Zimenezi zilembedwe chifukwa cha mibado ya mʼtsogolo,

19“Yehova anayangʼana pansi kuchokera ku malo ake opatulika mmwamba,

20kuti amve kubuwula kwa anthu a mʼndende,

21Kotero dzina la Yehova lidzalengezedwa mu Ziyoni

22pamene mitundu ya anthu ndi maufumu

23Iye anathyola mphamvu zanga pa nthawi ya moyo wanga;

24Choncho Ine ndinati:

25Pachiyambi Inu munakhazikitsa maziko a dziko lapansi

26Izi zidzatha, koma Inu mudzakhalapo;

27Koma Inu simusintha,

28Ana a atumiki anu adzakhala pamaso panu;

← Masalimo 101 Masalimo Masalimo 103 →