1Tamanda Yehova, iwe moyo wanga;
2Tamanda Yehova, iwe moyo wanga,
3Amene amakhululuka machimo ako onse
4amene awombola moyo wako ku dzenje
5amene akwaniritsa zokhumba zako ndi zinthu zabwino,
6Yehova amachita chilungamo
7Iye anadziwitsa Mose njira zake,
8Yehova ndi wachifundo ndi wokoma mtima,
9Iye sadzatsutsa nthawi zonse,
10satichitira molingana ndi machimo athu,
11Pakuti monga kumwamba kuli kutali ndi dziko lapansi,
12monga kummawa kutalikirana ndi kumadzulo,
13Monga bambo amachitira chifundo ana ake,
14pakuti Iye amadziwa momwe tinawumbidwira,
15Kunena za munthu, masiku ake ali ngati udzu,
16koma mphepo imawombapo ndipo silionekanso
17Koma kuchokera muyaya mpaka muyaya
18iwo amene amasunga pangano lake
19Yehova wakhazikitsa mpando wake waufumu mmwamba
20Tamandani Yehova, inu angelo ake,
21Tamandani Yehova, zolengedwa zonse zakumwamba,
22Tamandani Yehova, ntchito yake yonse