We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 103

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 102 Masalimo Masalimo 104 →

1Tamanda Yehova, iwe moyo wanga;

2Tamanda Yehova, iwe moyo wanga,

3Amene amakhululuka machimo ako onse

4amene awombola moyo wako ku dzenje

5amene akwaniritsa zokhumba zako ndi zinthu zabwino,

6Yehova amachita chilungamo

7Iye anadziwitsa Mose njira zake,

8Yehova ndi wachifundo ndi wokoma mtima,

9Iye sadzatsutsa nthawi zonse,

10satichitira molingana ndi machimo athu,

11Pakuti monga kumwamba kuli kutali ndi dziko lapansi,

12monga kummawa kutalikirana ndi kumadzulo,

13Monga bambo amachitira chifundo ana ake,

14pakuti Iye amadziwa momwe tinawumbidwira,

15Kunena za munthu, masiku ake ali ngati udzu,

16koma mphepo imawombapo ndipo silionekanso

17Koma kuchokera muyaya mpaka muyaya

18iwo amene amasunga pangano lake

19Yehova wakhazikitsa mpando wake waufumu mmwamba

20Tamandani Yehova, inu angelo ake,

21Tamandani Yehova, zolengedwa zonse zakumwamba,

22Tamandani Yehova, ntchito yake yonse

← Masalimo 102 Masalimo Masalimo 104 →