We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 104

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 103 Masalimo Masalimo 105 →

1Tamanda Yehova, iwe moyo wanga.

2Iye wadzifunditsa kuwala ngati chovala;

3ndipo wayika pa madzi mitanda ya chipinda chake.

4Amapanga mphepo kukhala amithenga ake,

5Anakhazikitsa dziko lapansi pa maziko ake;

6Munaliphimba ndi nyanja yozama ngati chovala;

7Koma pakudzudzula kwanu madzi anathawa,

8Inu munamiza mapiri,

9Inu munayika malire ndipo sangathe kudutsa,

10Iye achititsa akasupe kutulutsa madzi kupita ku zigwa;

11Iwo amapereka madzi kwa zirombo zonse zakuthengo;

12Mbalame zamlengalenga zimayika zisa mʼmbali mwa madzi;

13Iye amathirira mapiri kuchokera ku zipinda zake zapamwamba;

14Amameretsa udzu kuti ngʼombe zidye,

15vinyo amene amasangalatsa mtima wa munthu,

16Mitengo ya Yehova ndi yothiriridwa bwino,

17Mbalame zimamanga zisa zawo;

18Mapiri ataliatali ndi a mbalale;

19Mwezi umasiyanitsa nyengo

20Inu mumabweretsa mdima nukhala usiku,

21Mikango imabangula kufuna nyama,

22Dzuwa limatuluka ndipo iyo imapita kukabisala;

23Pamenepo munthu amapita ku ntchito yake,

24Ntchito zanu ndi zochulukadi Inu Yehova!

25Kuli nyanja yayikulu ndi yotambalala,

26Kumeneko sitima zapamadzi zimayenda uku ndi uku,

27Zonsezi zimayangʼana kwa Inu

28Mukazipatsa,

29Mukabisa nkhope yanu,

30Mukatumiza mzimu wanu,

31Ulemerero wa Yehova ukhalebe mpaka muyaya;

32Iye amene amayangʼana dziko lapansi ndipo limanjenjemera,

33Ine ndidzayimbira Yehova moyo wanga wonse;

34Zolingalira zanga zikhale zomukomera Iye,

35Koma anthu ochimwa awonongeke pa dziko lapansi

← Masalimo 103 Masalimo Masalimo 105 →