1Ine ndidzakutamandani, Inu Yehova, ndi mtima wanga wonse;
2Ndidzakondwa ndi kusangalala mwa inu;
3Adani anga amathawa,
4Pakuti Inu mwatsimikiza za kulungama kwanga ndi mlandu wanga;
5Mwadzudzula mitundu ya anthu ndipo mwawononga anthu oyipa;
6Chiwonongeko chosatha chagwera adani,
7Yehova akulamulira kwamuyaya;
8Iye adzaweruza dziko mwachilungamo;
9Yehova ndiye kothawirako kwa opsinjika mtima,
10Iwo amene amadziwa dzina lanu adzadalira Inu,
11Imbani nyimbo zamatamando kwa Yehova, ali pa mpando waufumu mu Ziyoni;
12Pakuti Iye amene amabwezera chilango akupha anzawo wakumbukira;
13Inu Yehova, onani momwe adani anga akundizunzira!
14kuti ndilengeze za matamando anu
15Mitundu ya anthu yagwa mʼdzenje limene yakumba;
16Yehova amadziwika ndi chilungamo chake;
17Oyipa amabwerera ku manda,
18Koma osowa sadzayiwalika nthawi zonse,
19Dzukani Inu Yehova, musalole munthu kuti apambane;
20Akantheni ndi mantha aakulu, Inu Yehova;