We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 9

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 8 Masalimo Masalimo 10 →

1Ine ndidzakutamandani, Inu Yehova, ndi mtima wanga wonse;

2Ndidzakondwa ndi kusangalala mwa inu;

3Adani anga amathawa,

4Pakuti Inu mwatsimikiza za kulungama kwanga ndi mlandu wanga;

5Mwadzudzula mitundu ya anthu ndipo mwawononga anthu oyipa;

6Chiwonongeko chosatha chagwera adani,

7Yehova akulamulira kwamuyaya;

8Iye adzaweruza dziko mwachilungamo;

9Yehova ndiye kothawirako kwa opsinjika mtima,

10Iwo amene amadziwa dzina lanu adzadalira Inu,

11Imbani nyimbo zamatamando kwa Yehova, ali pa mpando waufumu mu Ziyoni;

12Pakuti Iye amene amabwezera chilango akupha anzawo wakumbukira;

13Inu Yehova, onani momwe adani anga akundizunzira!

14kuti ndilengeze za matamando anu

15Mitundu ya anthu yagwa mʼdzenje limene yakumba;

16Yehova amadziwika ndi chilungamo chake;

17Oyipa amabwerera ku manda,

18Koma osowa sadzayiwalika nthawi zonse,

19Dzukani Inu Yehova, musalole munthu kuti apambane;

20Akantheni ndi mantha aakulu, Inu Yehova;

← Masalimo 8 Masalimo Masalimo 10 →