1Inu Yehova Ambuye athu,
2Kuchokera mʼkamwa mwa ana ndi makanda,
3Pamene ndilingalira za mayiko anu akumwamba,
4munthu ndani kuti Inu mumamukumbukira,
5Inu munamupanga kukhala wocheperapo kusiyana ndi zolengedwa zakumwamba
6Inu munamuyika wolamulira ntchito ya manja anu;
7nkhosa, mbuzi ndi ngʼombe pamodzi
8mbalame zamlengalenga
9Inu Yehova, Ambuye athu,