We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 7

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 6 Masalimo Masalimo 8 →

1Inu Yehova Mulungu wanga, Ine ndikuthawira kwa Inu;

2mwina angandikadzule ngati mkango,

3Inu Yehova Mulungu wanga,

4ngati ndachita zoyipa kwa iye amene ndili naye pa mtendere,

5pamenepo lolani adani anga andithamangitse ndi kundipitirira,

6Nyamukani Yehova, mu mkwiyo wanu;

7Lolani gulu la anthu a mitundu ina lisonkhane mokuzungulirani.

8Yehova aweruzeni anthu a mitundu inayo.

9Inu Mulungu wolungama,

10Chishango changa ndi Mulungu Wammwambamwamba,

11Mulungu amaweruza molungama,

12Ngati munthu satembenuka,

13Mulungu wakonza zida zake zoopsa;

14Taonani, munthu woyipa amalingalira zoyipa zokhazokha nthawi zonse.

15Iye amene akumba dzenje ndi kulizamitsa

16Mavuto amene amayambitsa amamubwerera mwini;

17Ine ndidzayamika Yehova chifukwa cha chilungamo chake;

← Masalimo 6 Masalimo Masalimo 8 →