1Inu Yehova Mulungu wanga, Ine ndikuthawira kwa Inu;
2mwina angandikadzule ngati mkango,
3Inu Yehova Mulungu wanga,
4ngati ndachita zoyipa kwa iye amene ndili naye pa mtendere,
5pamenepo lolani adani anga andithamangitse ndi kundipitirira,
6Nyamukani Yehova, mu mkwiyo wanu;
7Lolani gulu la anthu a mitundu ina lisonkhane mokuzungulirani.
8Yehova aweruzeni anthu a mitundu inayo.
9Inu Mulungu wolungama,
10Chishango changa ndi Mulungu Wammwambamwamba,
11Mulungu amaweruza molungama,
12Ngati munthu satembenuka,
13Mulungu wakonza zida zake zoopsa;
14Taonani, munthu woyipa amalingalira zoyipa zokhazokha nthawi zonse.
15Iye amene akumba dzenje ndi kulizamitsa
16Mavuto amene amayambitsa amamubwerera mwini;
17Ine ndidzayamika Yehova chifukwa cha chilungamo chake;