1Inu Yehova, musandidzudzule mu mkwiyo wanu,
2Ndichitireni chifundo Inu Yehova, pakuti ndalefuka;
3Moyo wanga uli pa mazunzo aakulu.
4Tembenukani Inu Yehova, ndipo mundilanditse;
5Palibe amene amakukumbukirani pamene wamwalira;
6Ine ndatopa ndi kubuwula;
7Maso anga atupa chifukwa cha chisoni;
8Chokani kwa ine inu nonse amene mumachita zoyipa,
9Yehova wamva kupempha kwanga kofuna chifundo;
10Adani anga onse adzachita manyazi ndipo adzakhala ndi mantha;