We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 6

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 5 Masalimo Masalimo 7 →

1Inu Yehova, musandidzudzule mu mkwiyo wanu,

2Ndichitireni chifundo Inu Yehova, pakuti ndalefuka;

3Moyo wanga uli pa mazunzo aakulu.

4Tembenukani Inu Yehova, ndipo mundilanditse;

5Palibe amene amakukumbukirani pamene wamwalira;

6Ine ndatopa ndi kubuwula;

7Maso anga atupa chifukwa cha chisoni;

8Chokani kwa ine inu nonse amene mumachita zoyipa,

9Yehova wamva kupempha kwanga kofuna chifundo;

10Adani anga onse adzachita manyazi ndipo adzakhala ndi mantha;

← Masalimo 5 Masalimo Masalimo 7 →