1Tcherani khutu ku mawu anga, Inu Yehova,
2Mverani kulira kwanga kofuna thandizo,
3Mmawa, Yehova mumamva mawu anga;
4Inu si Mulungu amene mumasangalala ndi zoyipa;
5Onyada sangathe kuyima pamaso panu;
6Mumawononga iwo amene amanena mabodza;
7Koma Ine, mwa chifundo chanu chachikulu,
8Tsogolereni Inu Yehova, mwa chilungamo chanu
9Palibe mawu ochokera mʼkamwa mwawo amene angadalirike;
10Lengezani kuti ndi olakwa, Inu Mulungu!
11Koma lolani kuti onse amene apeza chitetezo mwa Inu akondwere;
12Ndithu, Inu Yehova, mumadalitsa olungama;