We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 5

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 4 Masalimo Masalimo 6 →

1Tcherani khutu ku mawu anga, Inu Yehova,

2Mverani kulira kwanga kofuna thandizo,

3Mmawa, Yehova mumamva mawu anga;

4Inu si Mulungu amene mumasangalala ndi zoyipa;

5Onyada sangathe kuyima pamaso panu;

6Mumawononga iwo amene amanena mabodza;

7Koma Ine, mwa chifundo chanu chachikulu,

8Tsogolereni Inu Yehova, mwa chilungamo chanu

9Palibe mawu ochokera mʼkamwa mwawo amene angadalirike;

10Lengezani kuti ndi olakwa, Inu Mulungu!

11Koma lolani kuti onse amene apeza chitetezo mwa Inu akondwere;

12Ndithu, Inu Yehova, mumadalitsa olungama;

← Masalimo 4 Masalimo Masalimo 6 →