We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 4

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 3 Masalimo Masalimo 5 →

1Ndiyankheni pamene ndiyitana Inu,

2Anthu inu, mpaka liti mudzakhala mukusandutsa ulemerero wanga kukhala manyazi?

3Dziwani kuti Yehova wadziyikira padera anthu okhulupirika;

4Kwiyani koma musachimwe;

5Perekani nsembe zolungama

6Ambiri akufunsa kuti, “Ndani angationetse chabwino chilichonse?”

7Inu mwadzaza mtima wanga ndi chimwemwe chachikulu

8Ine ndidzagona ndi kupeza tulo mwamtendere,

← Masalimo 3 Masalimo Masalimo 5 →