1Ndiyankheni pamene ndiyitana Inu,
2Anthu inu, mpaka liti mudzakhala mukusandutsa ulemerero wanga kukhala manyazi?
3Dziwani kuti Yehova wadziyikira padera anthu okhulupirika;
4Kwiyani koma musachimwe;
5Perekani nsembe zolungama
6Ambiri akufunsa kuti, “Ndani angationetse chabwino chilichonse?”
7Inu mwadzaza mtima wanga ndi chimwemwe chachikulu
8Ine ndidzagona ndi kupeza tulo mwamtendere,