1Inu Yehova, achulukadi adani anga!
2Ambiri akunena za ine kuti,
3Koma Inu Yehova, ndinu chishango chonditeteza,
4Kwa Yehova, Ine ndilira mofuwula
5Ine ndimagona ndi kupeza tulo;
6Sindidzaopa adani anga osawerengeka amene
7Dzukani, Inu Yehova!
8Chipulumutso chimachokera kwa Yehova.