1Nʼchifukwa chiyani anthu a mitundu ina akufuna kuchita chiwembu?
2Mafumu a dziko lapansi akugwirizana nazo;
3Iwo akunena kuti, “Tiyeni timasule magoli awo
4Wokhala mmwamba akuseka;
5Ndipo iye awadzudzula mu mkwiyo wake
6“Ine ndakhazikitsa mfumu yanga
7Ine ndidzalengeza zimene Yehova walamula:
8Tandipempha,
9Iweyo udzawalamulira ndi ndodo yaufumu yachitsulo;
10Kotero, inu mafumu, chenjerani;
11Tumikirani Yehova mwa mantha
12Mpsopsoneni mwanayo kuti angakwiye;