We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 1

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

Masalimo Masalimo 2 →

1Wodala munthu

2Koma chikondwerero chake chili mʼmalamulo a Yehova

3Iye ali ngati mtengo wodzalidwa mʼmbali mwa mitsinje ya madzi,

4Sizitero ndi anthu oyipa!

5Kotero anthu oyipa sadzatha kuyima pa chiweruzo,

6Pakuti Yehova amayangʼanira mayendedwe a anthu olungama,

Masalimo Masalimo 2 →