1Iye wakhazikitsa maziko ake pa phiri loyera;
2Yehova amakonda zipata za Ziyoni
3Za ulemerero wako zimakambidwa,
4“Ndidzanena za Rahabe ndi Babuloni
5Ndithudi, za Ziyoni adzanena kuti,
6Yehova adzalemba mʼbuku la kawundula wa anthu a mitundu ina:
7Oyimba ndi ovina omwe adzati,