1Ndimvereni Yehova ndipo mundiyankhe,
2Yangʼanirani moyo wanga, pakuti ndine wodzipereka kwa Inu.
3Mundichitire chifundo, Inu Ambuye,
4Bweretsani chimwemwe kwa mtumiki wanu, Ambuye,
5Inu Ambuye, ndinu wokhululuka ndi wabwino,
6Yehova imvani pemphero langa;
7Pa tsiku la mavuto anga ndidzayitana Inu,
8Pakati pa milungu palibe wina wofanana nanu Ambuye;
9Mitundu yonse ya anthu imene munayipanga
10Pakuti ndinu wamkulu ndipo mumachita zodabwitsa;
11Ndiphunzitseni njira yanu Yehova,
12Ndidzakutamandani Ambuye Mulungu wanga, ndi mtima wanga wonse;
13Pakuti chikondi chanu nʼchachikulu kwa ine;
14Inu Mulungu wanga, anthu odzikuza akundithira nkhondo;
15Koma Ambuye ndinu Mulungu wachifundo ndi wokoma mtima,
16Tembenukirani kwa ine ndipo ndichitireni chifundo;
17Mundionetse chizindikiro cha ubwino wanu