1Malo anu okhalamo ndi okomadi,
2Moyo wanga ukulakalaka, mpaka kukomoka,
3Ngakhale timba wapeza nyumba yokhalamo,
4Odala amene amakhala mʼNyumba yanu;
5Odala amene mphamvu yawo ili mwa Inu,
6Pamene akudutsa chigwa cha Baka,
7Iwo amanka nakulirakulira mphamvu
8Imvani pemphero langa, Inu Yehova Mulungu Wamphamvuzonse;
9Yangʼanani chishango chathu, Inu Mulungu;
10Nʼkwabwino kukhala mʼmabwalo anu tsiku limodzi
11Pakuti Yehova Mulungu ndi dzuwa ndi chishango;
12Inu Yehova Wamphamvuzonse,