We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 84

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 83 Masalimo Masalimo 85 →

1Malo anu okhalamo ndi okomadi,

2Moyo wanga ukulakalaka, mpaka kukomoka,

3Ngakhale timba wapeza nyumba yokhalamo,

4Odala amene amakhala mʼNyumba yanu;

5Odala amene mphamvu yawo ili mwa Inu,

6Pamene akudutsa chigwa cha Baka,

7Iwo amanka nakulirakulira mphamvu

8Imvani pemphero langa, Inu Yehova Mulungu Wamphamvuzonse;

9Yangʼanani chishango chathu, Inu Mulungu;

10Nʼkwabwino kukhala mʼmabwalo anu tsiku limodzi

11Pakuti Yehova Mulungu ndi dzuwa ndi chishango;

12Inu Yehova Wamphamvuzonse,

← Masalimo 83 Masalimo Masalimo 85 →