1Mulungu akutsogolera msonkhano waukulu;
2“Mudzateteza osalungama mpaka liti,
3Tetezani anthu ofowoka ndi amasiye;
4Landitsani anthu ofowoka ndi osowa;
5“Iwo sadziwa kanthu, sazindikira kalikonse.
6“Ndinati, ‘Inu ndinu Mulungu,
7Koma mudzafa ngati anthu wamba;
8Dzukani Inu Mulungu, weruzani dziko lapansi,