1Imbani mwachimwemwe kwa Mulungu mphamvu yathu;
2Yambani nyimbo, imbani tambolini
3Imbani lipenga la nyanga ya nkhosa yayimuna pa mwezi watsopano,
4ili ndi lamulo kwa Israeli,
5Iye anapereka lamulolo kwa zidzukulu za Yosefe
6Iye akunena kuti, “Ine ndinachotsa zolemetsa pa mapewa awo;
7Pa mavuto anu munayitana ndipo ndinakulanditsani,
8“Imvani anthu anga, ndipo ndidzakuchenjezani
9Musadzakhale ndi mulungu wachilendo pakati panu;
10Ine ndine Yehova Mulungu wanu,
11“Koma anthu anga sanandimvere;
12Kotero ndinawasiya ndi mitima yawo yosamverayo
13“Anthu anga akanangondimvera,
14nʼkanafulumira motani kuti ndigonjetse adani awo
15Iwo amene amadana ndi Yehova akanakhwinyata pamaso pake,
16Koma inu mukanadyetsedwa tirigu wabwino kwambiri;