We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 80

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 79 Masalimo Masalimo 81 →

1Tcherani khutu Inu mʼbusa wa Israeli,

2kwa Efereimu, Benjamini ndi Manase.

3Tibwezereni mwakale Inu Mulungu;

4Inu Mulungu Wamphamvuzonse,

5Mwawadyetsa buledi wa misozi;

6Mwachititsa kuti tikhale gwero la mikangano pakati pa anansi athu,

7Tibwezereni mwakale Inu Mulungu Wamphamvuzonse,

8Munatulutsa mpesa kuchoka ku Igupto;

9Munawulimira munda wamphesawo,

10Mapiri anaphimbidwa ndi mthunzi wake,

11Unatambalitsa nthambi zake mpaka ku nyanja,

12Chifukwa chiyani mwagwetsa makoma ake

13Nguluwe zochokera mʼnkhalango zikuwononga

14Bweraninso kwa ife Inu Mulungu Wamphamvuzonse!

15muzu umene dzanja lanu lamanja ladzala,

16Mpesa wanu wadulidwa ndi kutenthedwa ndi moto;

17Dzanja lanu likhale pa munthu amene ali ku dzanja lanu lamanja,

18Ndipo ife sitidzatembenukira kumbali kuchoka kwa Inu;

19Tibwezereni mwakale Inu Yehova Mulungu Wamphamvuzonse

← Masalimo 79 Masalimo Masalimo 81 →