1Inu Mulungu, anthu a mitundu ina alowerera mʼcholowa chanu;
2Iwo anapereka mitembo ya atumiki anu
3Akhetsa magazi monga madzi
4Ife ndife chinthu chonyozeka kwa anansi athu,
5Mpaka liti Inu Yehova? Kodi mudzakwiya mpaka muyaya?
6Khuthulirani ukali wanu pa anthu a mitundu ina
7pakuti iwo ameza Yakobo
8Musatilange chifukwa cha machimo a makolo athu
9Tithandizeni Inu Mulungu Mpulumutsi wathu,
10Chifukwa chiyani anthu a mitundu ina akuti,
11Kubuwula kwa anthu a mʼndende kufike pamaso panu;
12Mubwezere kwa anansi athu kasanu nʼkawiri
13Pamenepo ife anthu anu, nkhosa za pabusa panu,