We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 79

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 78 Masalimo Masalimo 80 →

1Inu Mulungu, anthu a mitundu ina alowerera mʼcholowa chanu;

2Iwo anapereka mitembo ya atumiki anu

3Akhetsa magazi monga madzi

4Ife ndife chinthu chonyozeka kwa anansi athu,

5Mpaka liti Inu Yehova? Kodi mudzakwiya mpaka muyaya?

6Khuthulirani ukali wanu pa anthu a mitundu ina

7pakuti iwo ameza Yakobo

8Musatilange chifukwa cha machimo a makolo athu

9Tithandizeni Inu Mulungu Mpulumutsi wathu,

10Chifukwa chiyani anthu a mitundu ina akuti,

11Kubuwula kwa anthu a mʼndende kufike pamaso panu;

12Mubwezere kwa anansi athu kasanu nʼkawiri

13Pamenepo ife anthu anu, nkhosa za pabusa panu,

← Masalimo 78 Masalimo Masalimo 80 →