We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 78

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 77 Masalimo Masalimo 79 →

1Inu anthu anga imvani chiphunzitso changa;

2Ndidzatsekula pakamwa panga mʼmafanizo,

3zimene tinazimva ndi kuzidziwa,

4Sitidzabisira ana awo,

5Iye anapereka mawu wodzichitira umboni kwa Yakobo

6kotero kuti mʼbado wotsatira uthe kuzidziwa,

7Choncho iwo adzakhulupirira Mulungu

8Iwo asadzakhale monga makolo awo,

9Anthu a ku Efereimu, ngakhale ananyamula mauta,

10iwo sanasunge pangano la Mulungu

11Anayiwala zimene Iye anachita,

12Iyeyo anachita zodabwitsa makolo athu akuona,

13Anagawa nyanja pakati ndi kudutsitsapo iwowo,

14Anawatsogolera ndi mtambo masana

15Iye anangʼamba miyala mʼchipululu

16Anatulutsa mitsinje kuchokera mʼmingʼalu ya miyala

17Komabe iwowo anapitiriza kumuchimwira Iye,

18Ananyoza Mulungu mwadala

19Iwo anayankhula motsutsana naye ponena kuti,

20Iye atamenya thanthwe

21Yehova atawamva anakwiya kwambiri;

22pakuti iwo sanakhulupirire Mulungu

23Komabe Iye anapereka lamulo kwa mitambo mmwamba

24anagwetsa mana kuti anthu adye,

25Anthu anadya buledi wa angelo,

26Anamasula mphepo ya kummwera kuchokera kumwamba,

27Iye anawagwetsera nyama ngati fumbi,

28Anazibweretsa kwa iwo mʼkati mwa misasa yawo,

29Iwo anadya mpaka anatsala nazo zochuluka

30Koma iwowo anasiya kudya chakudya anachilakalakacho,

31mkwiyo wa Mulungu unawayakira;

32Ngakhale zinali chomwechi, iwo anapitirira kuchimwa;

33Kotero Mulungu anachepetsa masiku awo kuti azimirire ngati mpweya.

34Mulungu atawapha, iwo amamufunafuna Iyeyo;

35Ankakumbukira kuti Mulungu ndiye Thanthwe lawo,

36Komabe ankamuthyasika ndi pakamwa pawo,

37Mitima yawo sinali yokhazikika pa Iye,

38Komabe Iye anali wachifundo;

39Iye anakumbukira kuti iwo anali anthu chabe,

40Nthawi zambiri iwo ankamuwukira Iye mʼchipululu

41Kawirikawiri iwo ankamuyesa Mulungu;

42Sanakumbukire mphamvu zake,

43tsiku limene Iyeyo anaonetsa poyera zizindikiro zozizwitsa zake mu Igupto,

44Iye anasandutsa mitsinje yawo kukhala magazi;

45Iye anawatumizira magulu a ntchentche zimene zinawawononga,

46Iye anapereka mbewu zawo kwa ziwala,

47Iye anawononga mphesa zawo ndi matalala

48Iye anapereka ngʼombe zawo ku matalala,

49Anakhuthula moto wa ukali wake pa iwo,

50Analolera kukwiya,

51Anakantha ana oyamba kubadwa a Igupto,

52Koma Iye anatulutsa anthu ake ngati ziweto;

53Anawatsogolera bwinobwino kotero kuti analibe mantha

54Kotero anawafikitsa ku malire a dziko lake loyera,

55Iye anathamangitsa mitundu ya anthu patsogolo pawo

56Koma iwo anayesa Mulungu

57Anakhala okanika ndi osakhulupirika monga makolo awo,

58Anakwiyitsa Iyeyo ndi malo awo opembedzera mafano;

59Pamene Mulungu anamva zimenezi, anakwiya kwambiri;

60Anasiya nyumba ya ku Silo,

61Anatumiza mphamvu zake ku ukapolo,

62Anapereka anthu ake ku lupanga;

63Moto unanyeketsa anyamata awo,

64ansembe awo anaphedwa ndi lupanga,

65Kenaka Ambuye anakhala ngati akudzuka kutulo,

66Iye anathamangitsa adani ake;

67Kenaka Iye anakana matenti a Yosefe,

68Koma anasankha fuko la Yuda,

69Iye anamanga malo ake opatulika ngati zitunda,

70Anasankha Davide mtumiki wake

71kuchokera koyangʼanira nkhosa anamubweretsa

72Ndipo Davide anawaweta ndi mtima wolungama;

← Masalimo 77 Masalimo Masalimo 79 →