1Mulungu amadziwika mu Yuda;
2Tenti yake ili mu Salemu,
3Kumeneko Iye anathyola mivi yowuluka,
4Wolemekezeka ndinu,
5Anthu owuma mtima amagona atalandidwa chuma,
6Pa kudzudzula kwanu, Inu Mulungu wa Yakobo,
7Inu nokha ndiye muyenera kuopedwa.
8Kuchokera kumwamba Inu munalengeza chiweruzo,
9pamene Inu Mulungu munadzuka kuti muweruze,
10Zoonadi, ukali wanu pa anthu umakubweretserani matamando
11Chitani malumbiro kwa Yehova Mulungu wanu ndipo muwakwaniritse;
12Iye amaswa mzimu wa olamulira;