We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 75

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 74 Masalimo Masalimo 76 →

1Tikuthokoza Inu Mulungu,

2Mumati, “Ine ndimayika nthawi yoyenera,

3Pamene dziko lapansi ndi anthu ake onse anjenjemera,

4Kwa odzitama ndikuti, ‘Musadzitamenso,’

5Musatukule nyanga zanu motsutsana ndi kumwamba;

6Kugamula milandu sikuchokera kummawa kapena kumadzulo

7Koma ndi Mulungu amene amaweruza:

8Mʼdzanja la Yehova muli chikho

9Kunena za ine, ndidzalengeza izi kwamuyaya;

10Ndidzadula nyanga za onse oyipa

← Masalimo 74 Masalimo Masalimo 76 →