1Tikuthokoza Inu Mulungu,
2Mumati, “Ine ndimayika nthawi yoyenera,
3Pamene dziko lapansi ndi anthu ake onse anjenjemera,
4Kwa odzitama ndikuti, ‘Musadzitamenso,’
5Musatukule nyanga zanu motsutsana ndi kumwamba;
6Kugamula milandu sikuchokera kummawa kapena kumadzulo
7Koma ndi Mulungu amene amaweruza:
8Mʼdzanja la Yehova muli chikho
9Kunena za ine, ndidzalengeza izi kwamuyaya;
10Ndidzadula nyanga za onse oyipa