We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 74

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 73 Masalimo Masalimo 75 →

1Nʼchifukwa chiyani mwatitaya ife kwamuyaya, Inu Mulungu?

2Kumbukirani anthu amene munawagula kalekale,

3Tembenuzani mapazi kuloza ku mabwinja awa amuyaya

4Adani anu anabangula pa malo pamene Inu munkakumana nafe;

5Iwo anachita ngati anthu oti anyamula mbendera zawo

6Kenaka anaphwanya ndi nkhwangwa ndi akasemasema awo

7Iwo anatentha malo anu opatulika mpaka kuwagwetsa pansi;

8Ndipo anati mʼmitima yawo, “Tawatha kwathunthu.”

9Ife sitinapatsidwe chizindikiro chodabwitsa;

10Kodi mpaka liti, mdani adzanyoze Inu Mulungu?

11Chifukwa chiyani mukubweza dzanja lanu lamanja?

12Koma Inu Mulungu, ndinu Mfumu yanga kuyambira kalekale;

13Ndinu amene munagawa nyanja ndi mphamvu yanu;

14Ndinu amene munaphwanya mitu ya Leviyatani

15Ndinu amene munatsekula akasupe ndi mitsinje,

16Masana ndi anu ndipo usiku ndi wanunso;

17Ndinu amene munakhazikitsa malire onse a dziko lapansi;

18Kumbukirani momwe mdani wakunyozerani Inu Yehova,

19Musapereke moyo wa nkhunda yanu ku zirombo zakuthengo;

20Mukumbukire pangano lanu, pakuti malo obisika a mʼdziko

21Musalole kuti osautsidwa abwerere mwamanyazi;

22Dzukani Inu Mulungu ndipo dzitetezeni pa mlandu;

23Musalekerere phokoso la otsutsana nanu,

← Masalimo 73 Masalimo Masalimo 75 →