1Nʼchifukwa chiyani mwatitaya ife kwamuyaya, Inu Mulungu?
2Kumbukirani anthu amene munawagula kalekale,
3Tembenuzani mapazi kuloza ku mabwinja awa amuyaya
4Adani anu anabangula pa malo pamene Inu munkakumana nafe;
5Iwo anachita ngati anthu oti anyamula mbendera zawo
6Kenaka anaphwanya ndi nkhwangwa ndi akasemasema awo
7Iwo anatentha malo anu opatulika mpaka kuwagwetsa pansi;
8Ndipo anati mʼmitima yawo, “Tawatha kwathunthu.”
9Ife sitinapatsidwe chizindikiro chodabwitsa;
10Kodi mpaka liti, mdani adzanyoze Inu Mulungu?
11Chifukwa chiyani mukubweza dzanja lanu lamanja?
12Koma Inu Mulungu, ndinu Mfumu yanga kuyambira kalekale;
13Ndinu amene munagawa nyanja ndi mphamvu yanu;
14Ndinu amene munaphwanya mitu ya Leviyatani
15Ndinu amene munatsekula akasupe ndi mitsinje,
16Masana ndi anu ndipo usiku ndi wanunso;
17Ndinu amene munakhazikitsa malire onse a dziko lapansi;
18Kumbukirani momwe mdani wakunyozerani Inu Yehova,
19Musapereke moyo wa nkhunda yanu ku zirombo zakuthengo;
20Mukumbukire pangano lanu, pakuti malo obisika a mʼdziko
21Musalole kuti osautsidwa abwerere mwamanyazi;
22Dzukani Inu Mulungu ndipo dzitetezeni pa mlandu;
23Musalekerere phokoso la otsutsana nanu,