We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 73

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 72 Masalimo Masalimo 74 →

1Mulungu ndi wabwino ndithu kwa Israeli,

2Koma kunena za ine, mapazi anga anali pafupi kuterereka;

3Pakuti ndinkachitira nsanje odzitamandira,

4Iwo alibe zosautsa;

5Saona mavuto monga anthu ena;

6Nʼchifukwa chake kunyada kuli monga mkanda wa mʼkhosi mwawo;

7Mʼmitima yawo yokhota mumachokera zolakwa;

8Iwowo amanyogodola ndi kumayankhula zoyipa;

9Pakamwa pawo pamayankhula monyoza Mulungu kumwamba

10Nʼchifukwa chake anthu awo amapita kwa iwowo

11Iwo amati, “Kodi Mulungu angadziwe bwanji?

12Umu ndi mmene oyipa alili;

13Ndithudi ine ndawusunga pachabe mtima wanga woyera;

14Tsiku lonse ndapeza mavuto;

15Ndikanati, “Ndidzayankhula motere,”

16Pamene ndinayesa kuti ndimvetse zonsezi,

17kufikira nditalowa mʼmalo opatulika a Mulungu;

18Zoonadi Inu munawayika pa malo woterera;

19Mwamsangamsanga iwo amawonongedwa,

20Monga loto pamene wina adzuka,

21Pamene mtima wanga unasautsidwa

22ndinali wopusa ndi wosadziwa;

23Komabe ineyo ndili ndi Inu nthawi zonse;

24Inu mumanditsogolera ndi malangizo anu

25Kodi kumwamba ndili ndi yani kupatula Inu?

26Thupi ndi mtima wanga zitha kufowoka,

27Iwo amene ali kutali ndi Inu adzawonongeka;

28Koma kunena za Ine ndi kwabwino kukhala pafupi ndi Mulungu.

← Masalimo 72 Masalimo Masalimo 74 →