We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 72

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 71 Masalimo Masalimo 73 →

1Patsani mwana wa mfumu nzeru zanu zoweruzira mwa chilungamo,

2Iye adzaweruza anthu anu mwachilungamo,

3Mapiri adzabweretsa chuma kwa anthu anu,

4Iye adzateteza ozunzika pakati pa anthu

5Adzakhala ndi moyo pa mibado yonse,

6Iye adzakhala kugwa kwa mvula pa minda yolimidwa

7Mʼmasiku a munthu wolungama adzakhazikika;

8Iye adzalamulira kuchokera ku nyanja ina mpaka ku nyanja ina

9Mafuko a mʼchipululu adzawerama pamaso pake

10Mafumu a ku Tarisisi ndi a ku zilumba zakutali

11Mafumu onse adzamuweramira

12Pakuti iye adzawombola wosowa amene akulira,

13Iye adzachitira chifundo anthu ofowoka ndi anthu osowa

14Iye adzalanditsa iwo ku mazunzo ndi chiwawa

15Iye akhale ndi moyo wautali;

16Mulole kuti tirigu achuluke mʼdziko lonse;

17Dzina lake likhazikike kwamuyaya,

18Matamando akhale kwa Yehova Mulungu, Mulungu wa Israeli

19Matamando akhale ku dzina lake laulemerero kwamuyaya

20Uku ndiko kumaliza kwa mapemphero a Davide mwana wa Yese.

← Masalimo 71 Masalimo Masalimo 73 →