1Adzuke Mulungu, adani ake amwazikane;
2Monga momwe mphepo imachotsera utsi; Inu muwawulutsire kutali.
3Koma olungama asangalale
4Imbirani Mulungu imbirani dzina lake matamando,
5Atate wa ana amasiye, mtetezi wa akazi amasiye,
6Mulungu amakhazikitsa mtima pansi osungulumwa mʼmabanja,
7Pamene munatuluka kutsogolera anthu anu, Inu Mulungu,
8dziko lapansi linagwedezeka, miyamba inakhuthula pansi mvula,
9Munapereka mivumbi yochuluka, Inu Mulungu;
10Anthu anu anakhala mʼmenemo
11Ambuye analengeza mawu,
12“Mafumu ndi ankhondo anathawa mwaliwiro;
13Ngakhale mukugona pakati pa makola a ziweto,
14Pamene Wamphamvuzonse anabalalitsa mafumu mʼdziko,
15Mapiri a Basani ndi mapiri aulemerero;
16Muyangʼaniranji mwansanje inu mapiri a msonga zambiri,
17Magaleta a Mulungu ndi osawerengeka,
18Pamene Inu munakwera mmwamba,
19Matamando akhale kwa Ambuye, kwa Mulungu Mpulumutsi wathu
20Mulungu wathu ndi Mulungu amene amapulumutsa;
21Ndithu Mulungu adzaphwanya mitu ya adani ake,
22Ambuye akunena kuti, “Ndidzawabweretsa kuchokera ku Basani;
23Kuti muviyike mapazi anu mʼmagazi a adani anu,
24Mayendedwe aulemu a anthu anu aonekera poyera, Inu Mulungu;
25Patsogolo pali oyimba nyimbo pakamwa, pambuyo pawo oyimba nyimbo ndi zipangizo;
26Tamandani Mulungu mu msonkhano waukulu;
27Pali fuko lalingʼono la Benjamini, kuwatsogolera,
28Kungani mphamvu zanu Mulungu;
29Chifukwa cha Nyumba yanu ku Yerusalemu,
30Dzudzulani chirombo pakati pa mabango,
31Nthumwi zidzachokera ku Igupto;
32Imbirani Mulungu Inu mafumu a dziko lapansi
33Kwa Iye amene amakwera pa mitambo yakalekale ya mmwamba
34Lengezani za mphamvu za Mulungu,
35Ndinu woopsa, Inu Mulungu mʼmalo anu opatulika;