1Yehova atikomere mtima ndi kutidalitsa,
2Kuti njira zanu zidziwike pa dziko lapansi,
3Mitundu ya anthu ikutamandeni Inu Mulungu;
4Mitundu yonse ya anthu isangalale ndi kuyimba mwachimwemwe,
5Mitundu ya anthu ikutamandeni Inu Mulungu;
6Nthaka yabereka zokolola zake;
7Mulungu atidalitse