We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 67

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 66 Masalimo Masalimo 68 →

1Yehova atikomere mtima ndi kutidalitsa,

2Kuti njira zanu zidziwike pa dziko lapansi,

3Mitundu ya anthu ikutamandeni Inu Mulungu;

4Mitundu yonse ya anthu isangalale ndi kuyimba mwachimwemwe,

5Mitundu ya anthu ikutamandeni Inu Mulungu;

6Nthaka yabereka zokolola zake;

7Mulungu atidalitse

← Masalimo 66 Masalimo Masalimo 68 →