1Matamando akudikira Inu Mulungu mu Ziyoni;
2Inu amene mumamva pemphero,
3Pamene tinathedwa nzeru ndi machimo,
4Odala iwo amene inu muwasankha
5Mumatiyankha ife ndi ntchito zodabwitsa zachilungamo,
6amene munapanga mapiri ndi mphamvu zanu,
7Amene munakhalitsa bata nyanja
8Iwo amene akukhala kutali amaopa zizindikiro zozizwitsa zanu;
9Inu mumasamalira dziko lapansi ndi kulithirira;
10Mwadzaza nthaka yake ndi madzi ndi kusalaza migula yake,
11Inu mumaveka chaka ndi zinthu zochuluka,
12Malo a udzu a mʼchipululu amasefukira;
13Madambo akutidwa ndi zoweta