1Ndimvereni Mulungu pomwe ndikunena madandawulo anga;
2Ndibiseni ku chiwembu cha anthu oyipa,
3Iwo amanola malilime awo ngati malupanga,
4Iwo amaponya mivi yawo ali pa malo wobisala kwa munthu wosalakwa;
5Iwo amalimbikitsana wina ndi mnzake pa chikonzero chawo choyipa,
6Iwo amakonzekera zosalungama ndipo amati,
7Koma Mulungu adzawalasa ndi mivi;
8Iye adzatembenuza milomo yawoyo kuwatsutsa
9Anthu onse adzachita mantha;
10Lolani wolungama akondwere mwa Yehova