We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 64

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 63 Masalimo Masalimo 65 →

1Ndimvereni Mulungu pomwe ndikunena madandawulo anga;

2Ndibiseni ku chiwembu cha anthu oyipa,

3Iwo amanola malilime awo ngati malupanga,

4Iwo amaponya mivi yawo ali pa malo wobisala kwa munthu wosalakwa;

5Iwo amalimbikitsana wina ndi mnzake pa chikonzero chawo choyipa,

6Iwo amakonzekera zosalungama ndipo amati,

7Koma Mulungu adzawalasa ndi mivi;

8Iye adzatembenuza milomo yawoyo kuwatsutsa

9Anthu onse adzachita mantha;

10Lolani wolungama akondwere mwa Yehova

← Masalimo 63 Masalimo Masalimo 65 →