1Inu Mulungu, ndinu Mulungu wanga,
2Inu ndinakuonani ku malo anu opatulika
3Chifukwa chikondi chanu
4Ndidzakutamandani masiku onse a moyo wanga,
5Mudzakhutitsa moyo wanga ndi zonona.
6Pa bedi panga ndimakumbukira inu;
7Chifukwa ndinu thandizo langa,
8Moyo wanga umakangamira Inu;
9Iwo amene akufunafuna moyo wanga adzawonongedwa;
10Iwo adzaperekedwa ku lupanga
11Koma mfumu idzakondwera mwa Mulungu;