We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 62

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 61 Masalimo Masalimo 63 →

1Moyo wanga umapeza mpumulo mwa Mulungu yekha;

2Iye yekhayo ndiye thanthwe langa ndi chipulumutso changa;

3Kodi nonsenu mudzalimbana naye munthu mpaka liti?

4Iwo akufunitsitsa kumugwetsa

5Peza mpumulo mwa Mulungu yekhayo iwe moyo wanga;

6Iye yekhayo ndiye thanthwe langa ndi chipulumutso changa;

7Chipulumutso changa ndi ulemu wanga zimachokera kwa Mulungu:

8Dalirani Iye nthawi zonse, inu anthu;

9Anthu wamba ndi mpweya chabe;

10Musadalire kulanda mwachinyengo

11Mulungu wayankhula kamodzi,

12komanso Inu Ambuye, chikondi chanu nʼchosasinthika.

← Masalimo 61 Masalimo Masalimo 63 →