1Imvani kulira kwanga, Inu Mulungu;
2Kuchokera ku malekezero a dziko lapansi ine ndimayitana Inu
3Pakuti Inu mwakhala pothawirapo panga,
4Ine ndikulakalaka kukhala mʼtenti yanu kwamuyaya
5Pakuti Inu Mulungu mwamva malumbiro anga;
6Wonjezerani masiku a moyo wa mfumu,
7Iye akhale pa mpando waufumu pamaso pa Mulungu kwamuyaya;
8Kotero ndidzayimba matamando kwamuyaya pa dzina lanu