We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 61

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 60 Masalimo Masalimo 62 →

1Imvani kulira kwanga, Inu Mulungu;

2Kuchokera ku malekezero a dziko lapansi ine ndimayitana Inu

3Pakuti Inu mwakhala pothawirapo panga,

4Ine ndikulakalaka kukhala mʼtenti yanu kwamuyaya

5Pakuti Inu Mulungu mwamva malumbiro anga;

6Wonjezerani masiku a moyo wa mfumu,

7Iye akhale pa mpando waufumu pamaso pa Mulungu kwamuyaya;

8Kotero ndidzayimba matamando kwamuyaya pa dzina lanu

← Masalimo 60 Masalimo Masalimo 62 →