1Inu Mulungu mwatikanatu ife, ndipo mwatiwonongera otiteteza.
2Inu mwagwedeza dziko ndipo mwalingʼamba,
3Inu mwaonetsa anthu anu nthawi za mavuto;
4Koma kwa iwo amene amaopa Inu, Inu mwakweza mbendera
5Tipulumutseni ndi kutithandiza ndi dzanja lanu lamanja,
6Mulungu wayankhula kuchokera ku malo ake opatulika:
7Giliyadi ndi wanga, Manase ndi wanganso;
8Mowabu ndi mbale yanga yosambira,
9Adzandifikitse ndani ku mzinda wotetezedwa?
10Kodi si Inu Mulungu, Inu amene mwatikana ife
11Tipatseni chithandizo kuti tilimbane ndi mdani wathu,
12Chifukwa cha Mulungu, ife tidzapeza chipambano