We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 59

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 58 Masalimo Masalimo 60 →

1Landitseni kwa adani anga, Inu Mulungu;

2Landitseni kwa anthu ochita zoyipa

3Onani momwe iwo akundibisalira!

4Ine sindinachite cholakwa, koma iwo ndi okonzeka kundithira nkhondo.

5Inu Yehova Mulungu Wamphamvuzonse, Mulungu wa Israeli,

6Iwo amabweranso madzulo

7Onani zomwe amalavula mʼkamwa mwawo;

8Koma Inu Yehova, mumawaseka,

9Inu mphamvu yanga, ine ndiyangʼana kwa inu;

10Mulungu wanga wachikondi.

11Koma musawaphe, Inu Ambuye chishango chathu,

12Chifukwa cha machimo a pakamwa pawo

13muwawononge mu ukali (wanu)

14Iwo amabweranso madzulo,

15Iwo amayendayenda kufuna chakudya

16Koma ine ndidzayimba za mphamvu yanu,

17Inu mphamvu yanga, ndiyimba matamando kwa inu;

← Masalimo 58 Masalimo Masalimo 60 →