1Landitseni kwa adani anga, Inu Mulungu;
2Landitseni kwa anthu ochita zoyipa
3Onani momwe iwo akundibisalira!
4Ine sindinachite cholakwa, koma iwo ndi okonzeka kundithira nkhondo.
5Inu Yehova Mulungu Wamphamvuzonse, Mulungu wa Israeli,
6Iwo amabweranso madzulo
7Onani zomwe amalavula mʼkamwa mwawo;
8Koma Inu Yehova, mumawaseka,
9Inu mphamvu yanga, ine ndiyangʼana kwa inu;
10Mulungu wanga wachikondi.
11Koma musawaphe, Inu Ambuye chishango chathu,
12Chifukwa cha machimo a pakamwa pawo
13muwawononge mu ukali (wanu)
14Iwo amabweranso madzulo,
15Iwo amayendayenda kufuna chakudya
16Koma ine ndidzayimba za mphamvu yanu,
17Inu mphamvu yanga, ndiyimba matamando kwa inu;