1Kodi inu olamulira mumayankhuladi molungama?
2Ayi, mʼmitima mwanu mumakonzekera zosalungama,
3Ngakhale kuchokera tsiku lawo lobadwa oyipa amasochera;
4Ululu wawo uli ngati ululu wa njoka,
5Imene simva liwu la munthu wamatsenga,
6Gululani mano mʼkamwa mwawo, Inu Mulungu,
7Mulole kuti asowe ngati madzi oyenda
8Akhale ngati nkhono imene imasungunuka pamene ikuyenda;
9Miphika yanu isanagwire moto waminga ya mkandankhuku,
10Olungama adzasangalala poona kubwezera chilango,
11Ndipo anthu adzanena kuti,