We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 57

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 56 Masalimo Masalimo 58 →

1Mundichitire chifundo, Inu Mulungu mundichitire chifundo,

2Ine ndikufuwulira kwa Mulungu Wammwambamwamba,

3Mulungu amanditumizira kuchokera kumwamba ndi kundipulumutsa,

4Ine ndili pakati pa mikango,

5Mukwezekedwe Inu Mulungu, kuposa mayiko onse akumwamba;

6Iwo anatchera mapazi anga ukonde

7Mtima wanga ndi wokhazikika, Inu Mulungu

8Dzuka moyo wanga!

9Ndidzakutamandani Ambuye, pakati pa mitundu ya anthu,

10Pakuti chikondi chanu nʼchachikulu, kufikira ku mayiko akumwamba;

11Mukwezekedwe Inu Mulungu kuposa mayiko akumwamba,

← Masalimo 56 Masalimo Masalimo 58 →