1Mundichitire chifundo, Inu Mulungu mundichitire chifundo,
2Ine ndikufuwulira kwa Mulungu Wammwambamwamba,
3Mulungu amanditumizira kuchokera kumwamba ndi kundipulumutsa,
4Ine ndili pakati pa mikango,
5Mukwezekedwe Inu Mulungu, kuposa mayiko onse akumwamba;
6Iwo anatchera mapazi anga ukonde
7Mtima wanga ndi wokhazikika, Inu Mulungu
8Dzuka moyo wanga!
9Ndidzakutamandani Ambuye, pakati pa mitundu ya anthu,
10Pakuti chikondi chanu nʼchachikulu, kufikira ku mayiko akumwamba;
11Mukwezekedwe Inu Mulungu kuposa mayiko akumwamba,