1Mundichitire chifundo Inu Mulungu, pakuti anthu akundithamangitsa kwambiri;
2Ondinyoza akundithamangitsa tsiku lonse,
3Ndikachita mantha
4Mwa Mulungu, amene mawu ake ine ndimatamanda,
5Tsiku lonse amatembenuza mawu anga;
6Iwo amakambirana, amandibisalira,
7Musalole konse kuti athawe;
8Mulembe za kulira kwanga,
9Adani anga adzabwerera mʼmbuyo
10Mwa Mulungu amene mawu ake ndimawatamanda,
11mwa Mulungu ine ndimadalira ndipo sindidzachita mantha.
12Ndiyenera kuchita zomwe ndinalumbira kwa Mulungu;
13Pakuti mwawombola moyo wanga ku imfa