We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 56

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 55 Masalimo Masalimo 57 →

1Mundichitire chifundo Inu Mulungu, pakuti anthu akundithamangitsa kwambiri;

2Ondinyoza akundithamangitsa tsiku lonse,

3Ndikachita mantha

4Mwa Mulungu, amene mawu ake ine ndimatamanda,

5Tsiku lonse amatembenuza mawu anga;

6Iwo amakambirana, amandibisalira,

7Musalole konse kuti athawe;

8Mulembe za kulira kwanga,

9Adani anga adzabwerera mʼmbuyo

10Mwa Mulungu amene mawu ake ndimawatamanda,

11mwa Mulungu ine ndimadalira ndipo sindidzachita mantha.

12Ndiyenera kuchita zomwe ndinalumbira kwa Mulungu;

13Pakuti mwawombola moyo wanga ku imfa

← Masalimo 55 Masalimo Masalimo 57 →