1Mvetserani pemphero langa, Inu Mulungu,
2mverani ndipo mundiyankhe.
3chifukwa cha mawu a adani anga,
4Mtima wanga ukupweteka mʼkati mwanga;
5Mantha ndi kunjenjemera zandizinga;
6Ndinati, “Ndithu, ndikanakhala ndi mapiko ankhunda!
7Ndikanathawira kutali
8Ndikanathamangira kumalo anga a chitetezo;
9Sokonezani maganizo a oyipa, Inu Ambuye, tsutsani mawu awo;
10Usana ndi usiku iwo akuzungulirazungulira pa makoma ake;
11Mphamvu zowononga zili pa ntchito mu mzinda;
12Akanakhala mdani akundinyoza, ine
13Koma iweyo mnzanga, mnzanga woyenda naye,
14Mnzanga amene nthawi ina tinkasangalala
15Mulole imfa itenge adani anga mwadzidzidzi;
16Koma ine ndinafuwulira kwa Mulungu,
17Madzulo, mmawa ndi masana
18Iye amandiwombola ine osavulazidwa
19Mulungu amene ali pa mpando wake kwamuyaya,
20Mnzanga woyenda naye wathira nkhondo abwenzi ake;
21Mawu ake ndi osalala kuposa batala
22Tulani nkhawa zanu kwa Yehova
23Koma Inu Mulungu mudzawatsitsa anthu oyipa