We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 55

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 54 Masalimo Masalimo 56 →

1Mvetserani pemphero langa, Inu Mulungu,

2mverani ndipo mundiyankhe.

3chifukwa cha mawu a adani anga,

4Mtima wanga ukupweteka mʼkati mwanga;

5Mantha ndi kunjenjemera zandizinga;

6Ndinati, “Ndithu, ndikanakhala ndi mapiko ankhunda!

7Ndikanathawira kutali

8Ndikanathamangira kumalo anga a chitetezo;

9Sokonezani maganizo a oyipa, Inu Ambuye, tsutsani mawu awo;

10Usana ndi usiku iwo akuzungulirazungulira pa makoma ake;

11Mphamvu zowononga zili pa ntchito mu mzinda;

12Akanakhala mdani akundinyoza, ine

13Koma iweyo mnzanga, mnzanga woyenda naye,

14Mnzanga amene nthawi ina tinkasangalala

15Mulole imfa itenge adani anga mwadzidzidzi;

16Koma ine ndinafuwulira kwa Mulungu,

17Madzulo, mmawa ndi masana

18Iye amandiwombola ine osavulazidwa

19Mulungu amene ali pa mpando wake kwamuyaya,

20Mnzanga woyenda naye wathira nkhondo abwenzi ake;

21Mawu ake ndi osalala kuposa batala

22Tulani nkhawa zanu kwa Yehova

23Koma Inu Mulungu mudzawatsitsa anthu oyipa

← Masalimo 54 Masalimo Masalimo 56 →